19 Iye anandiuza kuti: “Iwe munthu wokondedwa kwambiri,+ usachite mantha.+ Mtendere ukhale nawe.+ Limba mtima, ndithu, limba mtima.”+ Atangolankhula nane, ndinadzilimbitsa ndipo pamapeto pake ndinati: “Lankhulani mbuyanga+ chifukwa inu mwandilimbikitsa.”+