Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 10:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pakuti Yehova Mulungu wanu ndi Mulungu wa milungu+ ndi Mbuye wa ambuye.+ Iye ndi Mulungu wamkulu, wamphamvu ndi woopsa,+ amene sakondera+ munthu aliyense ndipo salandira chiphuphu.+

  • Salimo 82:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 82 Mulungu waima pakati pa msonkhano wake,+

      Ndipo akuweruza pakati pa milungu kuti:+

  • Salimo 136:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Yamikani Mulungu wa milungu:+

      Pakuti kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena