Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 8:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Mfumuyo idzakula mphamvu koma osati mwa iyo yokha.+ Idzawononga zinthu zambiri+ ndipo chilichonse chimene izidzachita chidzaiyendera bwino. Idzawononga anthu amphamvu ndi anthu oyera.+

  • Mateyu 24:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Kenako anthu adzakuperekani ku chisautso+ ndipo adzakuphani.+ Mitundu yonse idzadana nanu+ chifukwa cha dzina langa.+

  • Chivumbulutso 11:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Zikamaliza kuchitira umboni wawo, chilombo chotuluka muphompho+ chidzachita nazo nkhondo, ndipo chidzazigonjetsa ndi kuzipha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena