Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 8:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Kenako ndinakhala malo amodzi ndi mneneri wamkazi ndipo iye anatenga pakati. Pambuyo pake anabereka mwana wamwamuna.+ Tsopano Yehova anandiuza kuti: “Um’patse dzina lakuti Maheri-salala-hasi-bazi,

  • Hoseya 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Yehova anandiuza kuti: “Yambanso kukonda mkazi wokondedwa ndi mwamuna,+ mkazi amene akuchita chigololo. Ukamukonde ngati mmene Yehova akukondera ana a Isiraeli,+ ngakhale kuti iwo akutembenukira kwa milungu ina,+ imene amakonda kuipatsa nsembe za mphesa zouma zoumba pamodzi.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena