Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 12:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Iye adzadula anthu onena kuti: “Ndi lilime lathu tidzapambana.+

      Timalankhula chilichonse chimene tikufuna ndi milomo yathu. Ndani angatilamulire?”

  • Salimo 73:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Kudzikweza kwawo kwafika kumwamba,+

      Akuyendayenda padziko lapansi ndipo lilime lawo likunena zilizonse zimene akufuna.+

  • Yesaya 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Yerusalemu wapunthwa ndipo Yuda wagwa,+ chifukwa lilime lawo ndiponso zochita zawo n’zotsutsana ndi Yehova.+ Iwo achita zinthu zomupandukira m’maso ake olemekezeka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena