Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 33:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Manase anatentha* ana ake aamuna pamoto+ m’chigwa cha mwana wa Hinomu,+ ndipo ankachita zamatsenga,+ ankawombeza,+ ankachita zanyanga,+ ndiponso anaika anthu olankhula ndi mizimu+ ndi olosera zam’tsogolo.+ Iye anachita zinthu zambiri zoipa pamaso pa Yehova ndiponso zomukwiyitsa.+

  • Habakuku 1:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Inu ndinu woyera kwambiri moti simungaonerere zinthu zoipa ndipo simungathe kuonerera khalidwe loipa.+ N’chifukwa chiyani mumayang’ana anthu amene amachita zachinyengo,+ ndipo n’chifukwa chiyani mukupitiriza kukhala chete pamene munthu woipa akumeza munthu amene ndi wolungama kuposa iyeyo?+

  • Malaki 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Mukapanda kumvera,+ ndiponso ngati simuganizira nkhani imeneyi mumtima mwanu+ kuti mulemekeze dzina langa,+ ndidzakutumizirani temberero+ ndi kutemberera madalitso anu.+ Ndatemberera dalitso la aliyense wa inu chifukwa simunaganizire nkhani imeneyi mumtima mwanu,” watero Yehova wa makamu.

  • 1 Akorinto 10:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Kapena “kodi tikufuna kuputa nsanje+ ya Yehova”? Kodi mphamvu zathu zingafanane ndi zake?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena