Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 10:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Pakuti ana a Isiraeli ndi ana a Alevi ayenera kubweretsa zopereka+ zambewu, vinyo watsopano+ ndi mafuta kuzipinda zodyera. Kumeneku ndi kumene kuli ziwiya za kumalo opatulika ndi ansembe amene anali kutumikira,+ olondera pazipata+ ndi oimba,+ ndipo tisanyalanyaze nyumba ya Mulungu wathu.+

  • Hagai 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 “Kodi ino ndi nthawi yoti inu muzikhala m’nyumba zokongoletsedwa ndi matabwa,+ nyumba iyi ili bwinja?+

  • Afilipi 2:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Pakuti ena onse akungofuna za iwo eni,+ osati za Khristu Yesu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena