Yeremiya 31:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 “Monga mmene ndakhalira ndikufunafuna mpata+ kuti ndiwazule, kuwagwetsa, kuwapasula, kuwawononga ndi kuwasakaza,+ ndidzakhalanso nawo tcheru kuti ndiwamange ndi kuwabzala,”+ watero Yehova. Yeremiya 32:31 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 31 ‘Mzinda uwu wakhala chinthu chondikwiyitsa+ ndi chondipsetsa mtima kuyambira pamene unamangidwa kufikira lero. Choncho ndiuchotsa pamaso panga,+ Malaki 3:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Kuyambira m’masiku a makolo anu mwakhala mukupatuka pa malamulo anga ndipo simunawasunge.+ Bwererani kwa ine ndipo ine ndibwerera kwa inu,”+ watero Yehova wa makamu. Koma inu mukunena kuti: “Tibwerere motani?”
28 “Monga mmene ndakhalira ndikufunafuna mpata+ kuti ndiwazule, kuwagwetsa, kuwapasula, kuwawononga ndi kuwasakaza,+ ndidzakhalanso nawo tcheru kuti ndiwamange ndi kuwabzala,”+ watero Yehova.
31 ‘Mzinda uwu wakhala chinthu chondikwiyitsa+ ndi chondipsetsa mtima kuyambira pamene unamangidwa kufikira lero. Choncho ndiuchotsa pamaso panga,+
7 Kuyambira m’masiku a makolo anu mwakhala mukupatuka pa malamulo anga ndipo simunawasunge.+ Bwererani kwa ine ndipo ine ndibwerera kwa inu,”+ watero Yehova wa makamu. Koma inu mukunena kuti: “Tibwerere motani?”