Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 21:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Uwu ndi uthenga wokhudza chipululu cha nyanja:*+ Kuchipululu kukubwera chinthu chinachake kuchokera kudziko lochititsa mantha.+ Chikubwera ngati mphepo yamkuntho+ yochokera kum’mwera.

  • Yesaya 66:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “Pakuti Yehova akubwera ngati moto,+ ndipo magaleta ake ali ngati mphepo yamkuntho+ kuti adzawabwezere mwaukali ndi mokwiya, ndiponso kuti adzawadzudzule ndi malawi a moto.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena