Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 75:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Anthu opusa ndinawauza kuti: “Musakhale opusa,”+

      Ndipo oipa ndinawauza kuti: “Musakweze nyanga.*+

  • Salimo 110:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Yehova amene ali kudzanja lako lamanja+

      Adzaphwanyaphwanya mafumu pa tsiku la mkwiyo wake.+

  • Luka 21:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Anthu adzaphedwa ndi lupanga ndiponso kutengedwa ukapolo kupita nawo ku mitundu ina yonse.+ Anthu a mitundu ina adzapondaponda Yerusalemu, kufikira nthawi zoikidwiratu+ za anthu a mitundu inawo zitakwanira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena