-
Salimo 2:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Mafumu a dziko lapansi aima pamalo awo,+
Ndipo nduna zapamwamba zasonkhana pamodzi mogwirizana.+
Atero kuti alimbane ndi Yehova+ komanso wodzozedwa wake.+
-
Chivumbulutso 11:18Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 Koma mitundu ya anthu inakwiya, ndipo mkwiyo wanu unafika. Inafikanso nthawi yoikidwiratu yakuti akufa aweruzidwe, nthawi yopereka mphoto+ kwa akapolo anu aneneri,+ ndiponso kwa oyerawo, ndi oopa dzina lanu, olemekezeka ndi onyozeka omwe.+ Komanso, nthawi yowononga+ amene akuwononga dziko lapansi.”+
-
-
-