Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Hoseya 12:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndinalankhula ndi aneneri+ ndipo ndinawaonetsa masomphenya ochuluka. Kudzera mwa aneneri, ndinali kupereka mafanizo ambiri.+

  • Amosi 3:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, sangachite kalikonse asanaulule chinsinsi chake kwa atumiki ake, aneneri.+

  • Mateyu 2:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Atafika kumeneko anakakhala mumzinda wotchedwa Nazareti+ kuti akwaniritsidwe mawu onenedwa kudzera mwa aneneri kuti: “Iye adzatchedwa Mnazareti.”+

  • Machitidwe 3:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Koma mwanjira imeneyi Mulungu wakwaniritsa zimene analengezeratu kudzera mwa aneneri onse, kuti Khristu wake adzavutika.+

  • Aroma 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Uthenga umenewu anaulonjeza kalekale kudzera mwa aneneri+ ake m’Malemba oyera.

  • Aheberi 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Kalekale, Mulungu analankhula ndi makolo athu nthawi zambiri+ ndiponso m’njira zambiri kudzera mwa aneneri.+

  • Yakobo 5:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Abale, pa nkhani ya kumva zowawa+ ndi kuleza mtima,+ tengerani chitsanzo+ kwa aneneri+ amene analankhula m’dzina la Yehova.+

  • 1 Petulo 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Aneneri amene analosera+ za kukoma mtima kwakukulu kumene munali kudzasonyezedwa,+ anafufuza za chipulumutso chimenechi mwakhama ndi mosamala.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena