Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 56:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Inu mwalemba za kuthawathawa kwanga.+

      Sungani misozi yanga m’thumba lanu lachikopa.+

      Kodi misozi yanga sili m’buku lanu?+

  • Salimo 69:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Afafanizidwe m’buku la anthu amoyo,+

      Ndipo iwo asalembedwe m’bukumo pamodzi ndi anthu olungama.+

  • Salimo 139:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Maso anu anandiona pamene ndinali mluza,+

      Ndipo ziwalo zanga zonse zinalembedwa m’buku lanu.

      M’bukumo munalembamo za masiku amene zinapangidwa+

      Koma panalibe ngakhale chiwalo chimodzi chimene chinali chitapangidwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena