Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 5:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Choncho iye anailola. Pamenepo mizimu yonyansayo inatuluka ndi kukalowa m’nkhumbazo, ndipo nkhumba zonsezo zinathamangira kuphedi ndi kulumphira m’nyanja. Nkhumbazo zinalipo pafupifupi 2,000, ndipo zinamira m’nyanjamo imodzi ndi imodzi.+

  • Luka 8:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Choncho ziwandazo zinatuluka mwa munthuyo ndi kukalowa munkhumbazo. Pamenepo nkhumba zonsezo zinathamangira kuphedi ndi kulumphira m’nyanja ndipo zinamira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena