Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 9:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndinayang’ana+ kwa Yehova Mulungu woona kuti ndimufunefune mwa kupemphera,+ kumuchonderera, kusala kudya, kuvala ziguduli* ndi kudzithira phulusa.+

  • Yona 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Uthengawo utafika kwa mfumu ya Nineve,+ mfumuyo inanyamuka pampando wake wachifumu ndi kuvula chovala chake chachifumu. Ndiyeno inavala chiguduli ndi kukhala paphulusa.+

  • Luka 10:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 “Tsoka iwe Korazini!+ Tsoka iwe Betsaida!+ Chifukwa ntchito zamphamvu zimene zinachitika kumeneko zikanachitika ku Turo ndi ku Sidoni, anthu kumeneko akanalapa kalekale atavala ziguduli n’kukhala paphulusa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena