Mateyu 12:46 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 46 Ali mkati molankhula ndi khamu la anthulo, kunabwera mayi ake ndi abale ake.+ Iwo anaima panja kufuna kuti alankhule naye. Yohane 2:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Izi zitatha, iye, mayi ake, abale ake+ ndi ophunzira ake anapita ku Kaperenao,+ koma kumeneko sanakhaleko masiku ambiri. Machitidwe 1:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Mogwirizana, onsewa analimbikira kupemphera,+ pamodzi ndi amayi ena+ komanso Mariya mayi a Yesu, limodzinso ndi abale ake a Yesu.+ 1 Akorinto 9:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Tili ndi ufulu wotenga alongo amene ndi akazi athu+ pa maulendo, mmene amachitira atumwi ena onse ndiponso abale a Ambuye+ komanso Kefa,+ si choncho kodi? Agalatiya 1:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Koma sindinaone mtumwi winanso kupatulapo Yakobo,+ m’bale+ wa Ambuye.
46 Ali mkati molankhula ndi khamu la anthulo, kunabwera mayi ake ndi abale ake.+ Iwo anaima panja kufuna kuti alankhule naye.
12 Izi zitatha, iye, mayi ake, abale ake+ ndi ophunzira ake anapita ku Kaperenao,+ koma kumeneko sanakhaleko masiku ambiri.
14 Mogwirizana, onsewa analimbikira kupemphera,+ pamodzi ndi amayi ena+ komanso Mariya mayi a Yesu, limodzinso ndi abale ake a Yesu.+
5 Tili ndi ufulu wotenga alongo amene ndi akazi athu+ pa maulendo, mmene amachitira atumwi ena onse ndiponso abale a Ambuye+ komanso Kefa,+ si choncho kodi?