Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 14:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Pamenepo mmodzi mwa anthuwo anamuuza kuti: “Bambo ako alumbirira anthu kuti, ‘Munthu aliyense wodya mkate lero ndi wotembereredwa!’”+ (Apa n’kuti anthuwo atayamba kutopa.)+

  • 1 Samueli 25:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Choncho Mulungu alange mowirikiza+ adani a Davide, ngati ine ndidzasiya munthu aliyense wa m’nyumba ya Nabala wokodzera khoma*+ ali wamoyo kufikira m’mawa.”+

  • Maliko 6:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndipo mwana wamkazi wa Herodiya analowa ndi kuvina, moti anasangalatsa Herode ndi ena amene anali kudya+ naye limodzi. Tsopano mfumu inauza mtsikanayo kuti: “Upemphe kwa ine chilichonse chimene ukufuna, ndipo ndidzakupatsa.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena