Levitiko 6:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 “‘Chilichonse chimene chingakhudze mnofu wake chidzakhala choyera,+ ndipo ngati munthu wadonthezera ena mwa magazi a nyamayo pachovala,+ chovala chimene wadonthezera magazicho muzichichapira kumalo oyera.+ Numeri 15:38 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 38 “Lankhula ndi ana a Isiraeli, uwauze kuti azisokerera mphonje m’mphepete mwa zovala zawo, ku mibadwo yawo yonse. Azisokereranso chingwe cha buluu pamwamba pa mphonje za zovalazo.+ Mateyu 9:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 chifukwa mumtima mwake anali kunena kuti: “Ndikangogwira malaya ake akunja okhawo, ndichira ndithu.”+ Maliko 3:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Popeza kuti anali atachiritsa anthu ambiri, onse amene anali ndi matenda aakulu anali kudziponya kwa iye kuti angomukhudza.+ Luka 6:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Onse m’khamulo anali kuyesetsa kuti amukhudze,+ chifukwa mphamvu+ zinali kutuluka mwa iye ndi kuchiritsa onsewo.
27 “‘Chilichonse chimene chingakhudze mnofu wake chidzakhala choyera,+ ndipo ngati munthu wadonthezera ena mwa magazi a nyamayo pachovala,+ chovala chimene wadonthezera magazicho muzichichapira kumalo oyera.+
38 “Lankhula ndi ana a Isiraeli, uwauze kuti azisokerera mphonje m’mphepete mwa zovala zawo, ku mibadwo yawo yonse. Azisokereranso chingwe cha buluu pamwamba pa mphonje za zovalazo.+
21 chifukwa mumtima mwake anali kunena kuti: “Ndikangogwira malaya ake akunja okhawo, ndichira ndithu.”+
10 Popeza kuti anali atachiritsa anthu ambiri, onse amene anali ndi matenda aakulu anali kudziponya kwa iye kuti angomukhudza.+
19 Onse m’khamulo anali kuyesetsa kuti amukhudze,+ chifukwa mphamvu+ zinali kutuluka mwa iye ndi kuchiritsa onsewo.