Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 65:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iye akutontholetsa phokoso la nyanja,+

      Akutontholetsa phokoso la mafunde ake komanso chipwirikiti cha mitundu ya anthu.+

  • Mateyu 8:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Koma iye anawafunsa kuti: “N’chifukwa chiyani mukuchita mantha chonchi, anthu achikhulupiriro chochepa inu?”+ Kenako anadzuka n’kudzudzula mphepo ndi nyanjayo, ndipo panachita bata lalikulu.+

  • Maliko 4:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Pamenepo anadzuka ndi kudzudzula mphepoyo ndi kuuza nyanjayo kuti: “Leka! Khala bata!”+ Chotero mphepoyo inaleka. Kenako panachita bata lalikulu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena