Mateyu 26:55 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 55 Mu ola lomwelo Yesu anafunsa khamu la anthulo kuti: “Bwanji mwabwera kudzandigwira mutatenga malupanga ndi zibonga ngati mukukalimbana ndi wachifwamba?+ Tsiku ndi tsiku ndinali kukhala pansi m’kachisi+ ndi kuphunzitsa, koma simunandigwire. Luka 4:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Komanso, anayamba kuphunzitsa m’masunagoge awo, ndipo anthu onse anali kumulemekeza.+ Luka 19:47 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 47 Ndipo anali kuphunzitsa m’kachisimo tsiku ndi tsiku. Koma ansembe aakulu, alembi ndi akuluakulu a anthu anafunitsitsa kumupha.+ Yohane 7:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Tsopano chikondwererocho chitafika pakatikati, Yesu analowa m’kachisi ndipo anayamba kuphunzitsa.+
55 Mu ola lomwelo Yesu anafunsa khamu la anthulo kuti: “Bwanji mwabwera kudzandigwira mutatenga malupanga ndi zibonga ngati mukukalimbana ndi wachifwamba?+ Tsiku ndi tsiku ndinali kukhala pansi m’kachisi+ ndi kuphunzitsa, koma simunandigwire.
47 Ndipo anali kuphunzitsa m’kachisimo tsiku ndi tsiku. Koma ansembe aakulu, alembi ndi akuluakulu a anthu anafunitsitsa kumupha.+
14 Tsopano chikondwererocho chitafika pakatikati, Yesu analowa m’kachisi ndipo anayamba kuphunzitsa.+