Yohane 13:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Mmodzi wa ophunzira ake amene Yesu anali kumukonda,+ anakhala patsogolo pa Yesu, pachifuwa chake. Yohane 21:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Zitatero, wophunzira amene Yesu anali kumukonda kwambiri uja+ anauza Petulo+ kuti: “Ndi Ambuye!” Pamenepo Simoni Petulo atamva kuti ndi Ambuye, anavala malaya ake ovala pamwamba, pakuti anali maliseche,* ndipo analumphira m’nyanja. Yohane 21:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Petulo atatembenuka, anaona wophunzira amene Yesu anali kumukonda+ akuwalondola. Wophunzira ameneyu ndi amene pa chakudya chamadzulo chija anatsamira pachifuwa cha Yesu ndi kumufunsa kuti: “Ambuye, ndani amene akufuna kukuperekani?”
7 Zitatero, wophunzira amene Yesu anali kumukonda kwambiri uja+ anauza Petulo+ kuti: “Ndi Ambuye!” Pamenepo Simoni Petulo atamva kuti ndi Ambuye, anavala malaya ake ovala pamwamba, pakuti anali maliseche,* ndipo analumphira m’nyanja.
20 Petulo atatembenuka, anaona wophunzira amene Yesu anali kumukonda+ akuwalondola. Wophunzira ameneyu ndi amene pa chakudya chamadzulo chija anatsamira pachifuwa cha Yesu ndi kumufunsa kuti: “Ambuye, ndani amene akufuna kukuperekani?”