Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 69:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Koma anandipatsa chomera chakupha kuti ndidye,+

      Ndipo anayesa kundimwetsa vinyo wowawasa pamene ndinali ndi ludzu.+

  • Mateyu 27:48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Nthawi yomweyo mmodzi wa iwo anathamanga kukatenga chinkhupule ndi kuchiviika m’vinyo wowawasa+ ndipo anachiika kubango ndi kum’patsa kuti amwe.+

  • Maliko 15:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Koma wina anathamanga kukaviika chinkhupule m’vinyo wowawasa, kenako anachiika kubango ndi kum’patsa kuti amwe,+ ndikunena kuti: “Mulekeni! Tione ngati Eliya angabwere kudzamutsitsa.”+ 

  • Luka 23:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Asilikali nawonso anamuchitira zachipongwe,+ anamuyandikira ndi kumupatsa vinyo wowawasa+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena