Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 19:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Choncho ku Makedoniya anatumizako awiri mwa anthu amene anali kumutumikira, omwe ndi Timoteyo+ ndi Erasito.+ Koma iye anatsalira m’chigawo cha Asia kwa kanthawi ndithu.

  • Aroma 16:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Wantchito mnzanga Timoteyo akupereka moni, chimodzimodzinso Lukiyo, Yasoni ndi Sosipato omwe ndi achibale anga.+

  • 1 Akorinto 4:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ndiye chifukwa chake ndikukutumizirani Timoteyo,+ popeza iye ndi mwana wanga wokondedwa ndi wokhulupirika+ mwa Ambuye. Iye adzakukumbutsani mmene ndimachitira zinthu potumikira Khristu Yesu,+ monga mmenenso ineyo ndikuphunzitsira kulikonse, mumpingo uliwonse.

  • 1 Atesalonika 3:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Chotero tinatumiza Timoteyo+ m’bale wathu ndi mtumiki wa Mulungu pa uthenga wabwino+ wonena za Khristu, kuti adzakulimbitseni ndi kukutonthozani pa chikhulupiriro chanu,

  • 1 Timoteyo 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 ndikulembera iwe Timoteyo,+ mwana wanga weniweni+ m’chikhulupiriro:

      Kukoma mtima kwakukulu, chifundo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate ndi Khristu Yesu Ambuye wathu, zikhale nawe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena