Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 1:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Choncho Yesu anachiritsa ambiri amene anali kudwala matenda osiyanasiyana,+ ndipo anatulutsa ziwanda zambiri. Koma sanalole kuti ziwandazo zilankhule, chifukwa zinali kum’dziwa kuti ndi Khristu.+

  • Luka 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Tsopano Yesu anasonkhanitsa atumwi 12 aja ndi kuwapatsa mphamvu ndi ulamuliro pa ziwanda zonse ndi kuti azitha kuchiritsa matenda.+

  • Luka 10:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Tsopano anthu okwana 70 aja anabwerera ali osangalala. Iwo anauza Yesu kuti: “Ambuye, ngakhale ziwanda zinatigonjera+ pamene tinagwiritsa ntchito dzina lanu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena