Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 5:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ngati chifukwa cha uchimo wa munthu mmodziyo+ imfa inalamulira monga mfumu+ kudzera mwa munthuyo, amene alandira kukoma mtima kwakukulu+ kochuluka ndiponso mphatso yaulere+ yaikuluyo ya chilungamo, adzakhala ndi moyo ndi kulamulira monga mafumu+ kudzera mwa munthu mmodziyu, Yesu Khristu.+

  • Aroma 6:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Chifukwa malipiro a uchimo ndi imfa,+ koma mphatso+ imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha+ kudzera mwa Khristu Yesu Ambuye wathu.+

  • Aefeso 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kudzera mwa iyeyu, tinamasulidwa ndi dipo* la magazi+ ake, inde, takhululukidwa+ machimo athu, malinga ndi chuma cha kukoma mtima kwake kwakukulu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena