Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aheberi 5:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 N’zoona kuti munayenera kukhala aphunzitsi+ pofika nthawi ino. Koma sizili choncho, ndipo mukufunikanso wina woti akuphunzitseni mfundo zoyambirira+ za m’mawu opatulika a Mulungu,+ kuyambira pa chiyambi. Inu mwakhala ngati munthu wofunika mkaka, osati chakudya chotafuna.+

  • Aheberi 5:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma chakudya chotafuna ndi cha anthu okhwima mwauzimu, amene pogwiritsa ntchito mphamvu zawo za kuzindikira,+ aphunzitsa mphamvuzo kusiyanitsa choyenera ndi chosayenera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena