Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 44:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Koma chifukwa cha inu, tikuphedwa nthawi zonse.

      Takhala ngati nkhosa zokaphedwa.+

  • Aroma 8:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Monga mmene Malemba amanenera kuti: “Chifukwa cha inu, tikuphedwa nthawi zonse. Takhala ngati nkhosa zokaphedwa.”+

  • 2 Akorinto 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 ngati osadziwika koma odziwika bwino,+ ngati oti tikufa koma tikukhalabe ndi moyo,+ ngati olangidwa+ koma osakaphedwa,+

  • Chivumbulutso 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Atamatula chidindo chachisanu, ndinaona pansi pa guwa lansembe+ pali miyoyo+ ya amene anaphedwa+ chifukwa cha mawu a Mulungu, ndiponso chifukwa cha ntchito yochitira umboni+ imene anali nayo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena