1 Timoteyo 1:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 ndiponso kuti asamamvere nkhani zonama+ ndi kukumbana mibadwo ya makolo. Zimenezi n’zosapindulitsa,+ koma zimangoyambitsa mafunso ndipo siziphunzitsa anthu chilichonse chochokera kwa Mulungu chokhudza chikhulupiriro. 1 Timoteyo 4:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Koma uzipewa nkhani zonama+ zimene zimaipitsa zinthu zoyera ndi zimene amayi okalamba amakamba. M’malomwake, ukhale ndi chizolowezi chochita zinthu zokuthandiza kuti ukhalebe wodzipereka kwa Mulungu.+ Tito 3:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Koma iwe pewa mafunso opusa,+ kukumba mibadwo ya makolo,+ mikangano+ ndi kulimbana pa za Chilamulo,+ chifukwa zimenezi n’zosapindulitsa ndiponso n’zachabechabe.
4 ndiponso kuti asamamvere nkhani zonama+ ndi kukumbana mibadwo ya makolo. Zimenezi n’zosapindulitsa,+ koma zimangoyambitsa mafunso ndipo siziphunzitsa anthu chilichonse chochokera kwa Mulungu chokhudza chikhulupiriro.
7 Koma uzipewa nkhani zonama+ zimene zimaipitsa zinthu zoyera ndi zimene amayi okalamba amakamba. M’malomwake, ukhale ndi chizolowezi chochita zinthu zokuthandiza kuti ukhalebe wodzipereka kwa Mulungu.+
9 Koma iwe pewa mafunso opusa,+ kukumba mibadwo ya makolo,+ mikangano+ ndi kulimbana pa za Chilamulo,+ chifukwa zimenezi n’zosapindulitsa ndiponso n’zachabechabe.