Yesaya 53:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Chifukwa cha kuvutika kwake, iye adzaona zabwino+ ndipo adzakhutira.+ Chifukwa cha zimene akudziwa, mtumiki wanga wolungamayo+ adzachititsa kuti anthu ambiri azionedwa olungama,+ ndipo adzasenza zolakwa zawo.+ Aroma 16:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Tsopano Mulungu+ angakulimbitseni mwa uthenga wabwino umene ndikulengeza ndiponso mwa uthenga wonena za Yesu Khristu umene ukulalikidwa. Uthenga wabwino umenewu ndi wogwirizana ndi zimene zaululidwa zokhudza chinsinsi chopatulika+ chimene chakhala chobisika kuyambira nthawi zakale. 2 Timoteyo 1:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Iye anatipulumutsa+ ndi kutiitana kuti tikhale oyera,+ osati chifukwa cha ntchito zathu,+ koma mwa chifuniro chake ndi kukoma mtima kwake kwakukulu. Iye anatikomera mtima m’njira imeneyi kalekalelo mwa Khristu Yesu.+
11 Chifukwa cha kuvutika kwake, iye adzaona zabwino+ ndipo adzakhutira.+ Chifukwa cha zimene akudziwa, mtumiki wanga wolungamayo+ adzachititsa kuti anthu ambiri azionedwa olungama,+ ndipo adzasenza zolakwa zawo.+
25 Tsopano Mulungu+ angakulimbitseni mwa uthenga wabwino umene ndikulengeza ndiponso mwa uthenga wonena za Yesu Khristu umene ukulalikidwa. Uthenga wabwino umenewu ndi wogwirizana ndi zimene zaululidwa zokhudza chinsinsi chopatulika+ chimene chakhala chobisika kuyambira nthawi zakale.
9 Iye anatipulumutsa+ ndi kutiitana kuti tikhale oyera,+ osati chifukwa cha ntchito zathu,+ koma mwa chifuniro chake ndi kukoma mtima kwake kwakukulu. Iye anatikomera mtima m’njira imeneyi kalekalelo mwa Khristu Yesu.+