Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 56:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ine ndimadalira Mulungu. Sindidzaopa.+

      Kodi munthu wochokera kufumbi angandichite chiyani?+

  • Salimo 118:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Yehova ali kumbali yanga, sindidzaopa.+

      Munthu wochokera kufumbi angandichite chiyani?+

  • Danieli 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ngati mungatiponyere m’ng’anjo yoyaka moto, Mulungu wathu amene tikumutumikira akhoza kutipulumutsa. Iye atipulumutsa m’ng’anjo yoyaka moto ndiponso m’manja mwanu mfumu.+

  • Luka 12:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Komanso ndikukuuzani ndithu, mabwenzi anga,+ Musamaope amene amapha thupi lokha, amene sangathe kuchita zoposa pamenepa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena