Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Afilipi 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Chotero, okondedwa anga, monga mmene mwakhalira omvera nthawi zonse,+ osati pokhapokha ine ndikakhalapo,* koma mofunitsitsa kwambiri tsopano pamene ine kulibe, pitirizani kukonza chipulumutso chanu, mwamantha+ ndi kunjenjemera.

  • 2 Timoteyo 2:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Chita chilichonse chotheka kuti usonyeze kuti ndiwe wovomerezeka+ pamaso pa Mulungu, wantchito+ wopanda chifukwa chochitira manyazi+ ndi ntchito imene wagwira, ndiponso wophunzitsa ndi kufotokoza bwino mawu a choonadi.+

  • Aheberi 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chotero, tiyeni tichite chilichonse chotheka kuti tilowe mu mpumulo umenewo, kuopera kuti wina angagwe ndi kutengera chitsanzo cha kusamvera cha makolo athuwo.+

  • Yuda 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Okondedwa,+ ngakhale kuti ndinali kuyesetsa kuti ndikulembereni za chipulumutso chimene tonsefe tili nacho,+ ndaona kuti ndi bwino kuti ndikulembereni zokulimbikitsani kumenya mwamphamvu nkhondo yachikhulupiriro+ chomwe chinaperekedwa kamodzi kokha kwa oyerawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena