Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 119:105
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 105 Mawu anu ndi nyale younikira kumapazi anga,+

      Ndi kuwala kounikira njira yanga.+

  • Yohane 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Kuwala+ kwenikweni kumene kumaunikira+ anthu osiyanasiyana+ kunali pafupi kubwera m’dziko.

  • Yohane 5:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Munthu ameneyu anali nyale yoyaka ndi yowala, ndipo kwa kanthawi kochepa inu munali ofunitsitsa kusangalala m’kuwala kwakeko.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena