Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 23:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mzimu wa Yehova unandilankhulitsa,+

      Ndipo mawu ake anali palilime langa.+

  • Machitidwe 1:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Amuna inu, abale, kudzera pakamwa pa Davide, mzimu woyera+ unaneneratu lemba lokhudza Yudasi,+ amene anatsogolera anthu okagwira Yesu.+ Kunali kofunikira kuti lembalo likwaniritsidwe+

  • Machitidwe 28:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Choncho, popeza anali kutsutsana okhaokha, anayamba kuchoka, koma Paulo ananenabe mawu amodzi awa:

      “Mzimu woyera unanena zoona kwa makolo anu kudzera mwa Yesaya mneneri.

  • 1 Petulo 1:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Anali kufufuza nyengo+ yake kapena mtundu wa nyengo imene mzimu+ umene unali mwa iwo unali kuwasonyeza yokhudzana ndi Khristu.+ Mzimuwo unali kuchitira umboni za masautso a Khristu+ ndi za ulemerero+ wobwera pambuyo pake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena