Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Tikudziwa kuti pamene tsopano Khristu waukitsidwa kwa akufa,+ sadzafanso.+ Imfa sikuchitanso ufumu pa iye.

  • 1 Timoteyo 6:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Iye yekha ndiye amene ali ndi moyo wosakhoza kufa,+ amene amakhala m’kuwala kosafikirika.+ Palibe munthu ndi mmodzi yemwe amene anamuonapo kapena amene angamuone.+ Iye apatsidwe ulemu+ ndipo mphamvu zake zikhalebe kosatha. Ame.

  • Aheberi 7:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Koma iye chifukwa chokhala ndi moyo kosatha,+ palibe omulowa m’malo pa unsembe wake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena