Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 8:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Kenako Mose anatenga chidale nʼkuchiyendetsa uku ndi uku monga nsembe yoyendetsa uku ndi uku yoperekedwa kwa Yehova.+ Chidale chimenechi anachitenga pa nkhosa yowaikira kuti akhale ansembe ndipo chinakhala gawo la Mose, mogwirizana ndi zimene Yehova analamula Mose.+

  • Salimo 99:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Mose ndi Aroni anali mʼgulu la ansembe ake,+

      Ndipo Samueli anali mʼgulu la anthu amene ankaitana pa dzina lake.+

      Iwo ankaitana Yehova,

      Ndipo iye ankawayankha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena