28 Utumiki umene mabanja a ana a Gerisoni azichita mʼchihema chokumanako+ ndi umenewu. Itamara+ mwana wa wansembe Aroni, ndi amene aziyangʼanira utumiki wawo.
8 Ana a Merari anawapatsa ngolo 4 ndi ngʼombe zamphongo 8, mogwirizana ndi zimene zinkafunika pa ntchito yawo imene ankagwira moyangʼaniridwa ndi Itamara, mwana wa wansembe Aroni.+