Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 9:16-18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kodi mukuona kuti mwachita bwino kuika Abimeleki kukhala mfumu?+ Kodi mwachita zimenezi kuchokera pansi pa mtima? Nanga Yerubaala ndi banja lake mwamuchitira zabwino? Kodi zimene mwamuchitira ndi zogwirizana ndi zimene iye anachita? 17 Pamene bambo anga anakumenyerani nkhondo,+ anaika moyo wawo pangozi kuti akulanditseni kwa Amidiyani.+ 18 Koma inu lero mwaukira banja la bambo anga ndipo mwapha ana awo aamuna 70 pamwala umodzi.+ Kenako mwaika Abimeleki, mwana wa kapolo wake wamkazi,+ kukhala mfumu ya atsogoleri a ku Sekemu chifukwa chongoti ndi mchimwene wanu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena