-
Yesaya 56:12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
Mawa lidzakhalanso ngati lero, mwinanso kuposa pamenepa.”
-
-
Luka 12:19Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
19 ndiye ndidzadziuza kuti: “Uli ndi zinthu zambiri zabwino ndipo zisungika kwa zaka zambiri. Mtima mʼmalo, udye, umwe ndi kusangalala.”’
-