Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ine ndidzagona pansi nʼkupeza tulo,

      Ndipo ndidzadzuka ndili wotetezeka,

      Chifukwa Yehova akupitiriza kundithandiza.+

  • Miyambo 3:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ukagona sudzaopa chilichonse.+

      Udzagona ndithu, ndipo tulo tako tidzakhala tokoma.+

  • Miyambo 3:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Chifukwa uzidzadalira kwambiri Yehova,+

      Ndipo adzateteza phazi lako kuti lisakodwe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena