Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 11:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Poyankha Yesu anawauza kuti: “Pitani mukauze Yohane zimene mukumva ndi kuona:+ 5 Amene anali ndi vuto losaona akuona,+ olumala akuyenda, akhate+ akuyeretsedwa ndipo amene anali ndi vuto losamva akumva. Akufa akuukitsidwa ndipo osauka akuuzidwa uthenga wabwino.+

  • Machitidwe 10:37, 38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Inu mukudziwa nkhani imene inali mʼkamwamʼkamwa kuyambira ku Galileya+ mpaka ku Yudeya konse, pambuyo pa ubatizo umene Yohane ankalalikira. 38 Nkhani yake inali yonena za Yesu wa ku Nazareti, amene Mulungu anamudzoza ndi mzimu woyera+ ndi mphamvu. Popeza Mulungu anali naye,+ anayenda mʼdziko lonse nʼkumachita zabwino ndiponso kuchiritsa anthu onse amene Mdyerekezi+ ankawazunza.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena