Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 23:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 “Kenako ndidzasonkhanitsa pamodzi nkhosa zanga zotsala kuchokera mʼmayiko onse kumene ndinazibalalitsira+ ndipo ndidzazibwezeretsa kumalo awo kumene zimadyera.+ Nkhosazo zidzaberekana ndi kuchuluka.+

  • Yeremiya 23:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Mʼmasiku a mfumu imeneyi, Yuda adzapulumutsidwa+ ndipo Isiraeli adzakhala motetezeka.+ Dzina la mfumuyi lidzakhala: Yehova Ndi Chilungamo Chathu.”+

  • Yeremiya 30:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma iwe Yakobo mtumiki wanga usachite mantha,” akutero Yehova,

      “Ndipo iwe Isiraeli usaope.+

      Chifukwa ndidzakupulumutsa kuchokera kutali

      Ndidzapulumutsanso ana ako kuchokera kudziko limene anatengedwa kukakhala akapolo.+

      Yakobo adzabwerera ndipo adzakhala mosatekeseka komanso mopanda zosokoneza.

      Sipadzakhala wowaopseza.+

      11 Chifukwa ine ndili ndi iwe kuti ndikupulumutse,” akutero Yehova.

      “Ndidzawononga anthu a mitundu yonse yakumene ndinakubalalitsirani.+

      Koma iweyo sindidzakuwononga.+

      Ndidzakulanga* pamlingo woyenera,

      Ndipo sindidzakusiya osakupatsa chilango.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena