Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 37:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Atatero Yakobo anangʼamba zovala zake nʼkuvala chiguduli mʼchiuno mwake, ndipo anamulira mwana wake masiku ambiri.

  • Yesaya 15:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Iye wapita kukachisi ndi ku Diboni,+

      Wapita kumalo okwezeka kukalira.

      Mowabu akulira mofuula chifukwa cha zimene zachitikira Nebo+ ndi Medeba.+

      Mutu uliwonse aumeta mpala+ ndipo ndevu zonse zametedwa.+

       3 Anthu avala ziguduli mʼmisewu yake.

      Pamadenga awo komanso mʼmabwalo a mizinda yawo, onse akulira mofuula.

      Akulira nʼkumapita kumunsi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena