Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 40:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Atandilowetsa mʼbwalo lamkati kudzera kumʼmawa, anayeza kanyumba kapagetiko ndipo anapeza kuti miyezo yake ndi yofanana ndi ya tinyumba tina tija.

  • Ezekieli 40:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Khonde lake linayangʼana kubwalo lakunja ndipo pazipilala zake zamʼmbali panali zithunzi za mtengo wa kanjedza ndipo anthu akafuna kulowa mʼkanyumbako amakwera masitepe 8.

  • Ezekieli 40:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Kenako anandipititsa kugeti la kumpoto.+ Atayeza kanyumba kapagetiko, anapeza kuti miyezo yake inali yofanana ndi ya tinyumba tina tija.

  • Ezekieli 40:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Zipilala zake zamʼmbali zinayangʼana kubwalo lakunja ndipo pazipilala zonsezo panali zithunzi za mtengo wa kanjedza. Anthu akafuna kulowa mʼkanyumbako amakwera masitepe 8.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena