Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 28:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mwadzidzidzi Yesu anakumana nawo nʼkunena kuti: “Moni azimayi!” Kenako iwo anafika pafupi nʼkugwira mapazi ake ndipo anamuweramira mpaka nkhope zawo pansi.

  • Yohane 20:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Madzulo a tsiku limenelo, limene linali tsiku loyamba la mlungu, ophunzirawo anasonkhana pamodzi. Mʼnyumba imene anasonkhanayo anakhoma zitseko chifukwa ankaopa Ayuda. Koma Yesu analowa nʼkuima pakati pawo ndipo anawauza kuti: “Mtendere ukhale nanu.”+

  • 1 Akorinto 15:4-7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiponso kuti anaikidwa mʼmanda,+ kenako anaukitsidwa+ pa tsiku lachitatu,+ mogwirizana ndi Malemba.+ 5 Panalinso zoti anaonekera kwa Kefa,*+ kenako kwa atumwi 12 aja.+ 6 Ndiyeno anaonekeranso kwa abale oposa 500 pa nthawi imodzi,+ ndipo ambiri a iwo tidakali nawo, koma ena anagona mu imfa. 7 Atatero anaonekera kwa Yakobo,+ kenako kwa atumwi onse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena