Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aefeso 3:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Zimenezi nʼzogwirizana ndi cholinga chamuyaya chimene iye anakhala nacho chokhudza Khristu,+ yemwe ndi Yesu Ambuye wathu. 12 Kudzera mwa iye, tili ndi ufulu wa kulankhulawu ndiponso timatha kufika kwa Mulungu mosavuta+ komanso popanda kukayikira chifukwa timakhulupirira Yesu.

  • Aheberi 10:19-22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Choncho abale, timalimba mtima kulowa mʼmalo oyera+ chifukwa cha magazi a Yesu. 20 Iye ndi amene anatitsegulira njira imeneyi yomwe ndi yatsopano komanso yamoyo ndipo imadutsa katani yotchingira,+ imene ndi thupi lake. 21 Popeza tili ndi wansembe wamkulu kwambiri woyangʼanira nyumba ya Mulungu,+ 22 tiyeni tifike kwa Mulungu ndi mtima wonse komanso tili ndi chikhulupiriro chonse, chifukwa mitima yathu yayeretsedwa* kuti tisakhalenso ndi chikumbumtima choipa,+ ndipo matupi athu asambitsidwa mʼmadzi oyera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena