Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 2:3-6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Komanso ukapempha kuti ukhale womvetsa zinthu+

      Ndi kuchonderera kuti ukhale wozindikira,+

       4 Ukapitiriza kuzifunafuna ngati siliva,+

      Ndi kuzifufuza ngati chuma chobisika,+

       5 Udzamvetsa tanthauzo la kuopa Yehova+

      Ndipo udzamudziwadi Mulungu.+

       6 Chifukwa Yehova ndi amene amapereka nzeru.+

      Kudziwa zinthu komanso kuzindikira zimatuluka mʼkamwa mwake.

  • Yohane 15:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Mukapitiriza kukhala ogwirizana ndi ine ndipo mawu anga akakhala mwa inu, mukhoza kupempha chilichonse chimene mukufuna ndipo chidzachitika kwa inu.+

  • 1 Yohane 5:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndipotu ife sitikayikira*+ kuti chilichonse chimene tingamupemphe mogwirizana ndi zimene amafuna, amatimvera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena