Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • rsg19
  • Thanzi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Thanzi
  • Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
  • Timitu
  • Thupi la Munthu
  • Kukhala ndi Thanzi Labwino
  • Matenda Ndiponso Mmene Thanzi la Munthu Lilili
  • Kukhala Woyembekezera, Kubereka ndi Kusamalira Mwana
  • Ukalamba
  • Kusamalira Odwala
  • Zizolowezi Zoipa
Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019
rsg19

Thanzi

Zimene Baibulo Limanena: Thanzi Lathu Galamukani!, 4/2013

❐ Galamukani!, 2/8/2005

Zimene Zikuchitikira Madokotala M’dziko Limene Likusinthali

Madokotala Amakumana N’zambiri

Kodi Udokotala Uli ndi Tsogolo Lotani?

Chifukwa Chake Anthufe Timadwala Mphunzitsi Waluso, mutu 23

Thupi la Munthu

Tinapangidwa Modabwitsa’ Galamukani!, 5/2011

N’zotheka Ndithu Kuchepetsa Vuto la Kuiwala Galamukani!, 2/2009

‘Tinapangidwa Modabwitsa’ Nsanja ya Olonda, 6/15/2007

Kukongola ndi Kaonekedwe

Kodi Ndiyeneradi Kudandaula Ndi Mmene Ndimaonekera? Mayankho a Mafunso 10, funso 2

Zimene Baibulo Limanena: Kukongola Galamukani!, Na. 4 2016

❐ Galamukani!, 1/8/2005

Kuipa Kofunitsitsa Kukhala Wokongola

Kukongola Kofunika Kwambiri

Nkhawa Imene Munthu Ali Nayo pa Maonekedwe Ake Ikasanduka Matenda Galamukani!, 8/8/2004

Ziwalo za Thupi ndi Mmene Zimagwirira Ntchito

Kodi Mumadziwa Kuti Tili ndi Mitsempha Ina Imene Imagwira Ntchito Ngati Ubongo? Galamukani!, Na. 3 2017

Misozi Yathu Ndi Yodabwitsa Kwambiri Galamukani!, 3/2014

Muziyamikira Mphatso Zimene Muli Nazo Galamukani!, 5/2011

Kodi Mungadziwe Bwanji Kuti Muli ndi Matenda a Chithokomiro? Galamukani!, 5/2009

Dzitetezeni Kuti Musagonthe M’kutu! Galamukani!, 6/8/2002

Kukhala ndi Thanzi Labwino

❐ Galamukani!, Na. 6 2016

Kodi Tingapewe Bwanji Matenda?

Dzitetezeni ku Matenda

Zimene Mungachite Kuti Mukhale ndi Moyo Wathanzi Galamukani!, 6/2015

Kamphepo Kayaziyazi Komanso Dzuwa Ndi Mankhwala Galamukani!, 3/2015

❐ Galamukani!, 3/2011

Pali Zimene Mungachite Kuti Mukhale ndi Thanzi Labwino

1​—Muzidya Zakudya Zoyenera

2​—Muzisamalira Thupi Lanu

3​—Muzichita Masewera Olimbitsa Thupi

4​—Muziteteza Thanzi Lanu

5​—Muzikhala Wokonzeka Kusintha

Chitani Zinthu Zokuthandizani Kukhala ndi Thanzi Labwino

N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kusamalira Thanzi Langa? Achinyamata Amafunsa, Buku Loyamba, mutu 10

Zimene Achinyamata Amadzifunsa: N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kusamalira Thanzi Langa? Galamukani!, 6/2010

Kodi Pali Vuto Lililonse ndi Kukhalitsa Padzuwa? Galamukani!, 6/2009

N’chifukwa Chiyani Muyenera Kumakaonana ndi Dokotala wa Mano? Galamukani!, 5/2007

Tetezani Khungu Lanu Galamukani!, 6/8/2005

Mmene Kukonda Zinthu Zauzimu Kumakhudzira Moyo Wanu Nsanja ya Olonda, 2/1/2004

Njira Zisanu ndi Imodzi Zosamalira Thanzi Lanu Galamukani!, 10/8/2003

Zimene Mumasankha Zimakhudza Thanzi Lanu Galamukani!, 9/8/2003

Ukhondo

N’zotheka Kuthana ndi Nsikidzi Galamukani!, 12/2012

Matenda Amene Anavuta Kwambiri M’zaka za M’ma 1800 Galamukani!, 10/2010

N’chifukwa Chiyani Ukhondo Uli Wofunika? Nsanja ya Olonda, 12/1/2008

Mulungu Amakonda Anthu Oyera (Kamutu:  Kodi Tingatani Kuti Tikhale Aukhondo?) ‘Mulungu Apitirize Kukukondani,’ mutu 8

Sopo ndi “Katemera Amene Mungadzipatse Nokha” Galamukani!, 12/8/2003

Anatiyeretsa Kuti Tichite Ntchito Zokoma (Kamutu: Timadziwika ndi Ukhondo wa Pathupi ndi Panyumba) Nsanja ya Olonda, 6/1/2002

❐ Nsanja ya Olonda, 2/1/2002

Kodi Ukhondo Ndi Wofunika Motani?

Kodi Ukhondo Umatanthauza Chiyani Makamaka?

Masewera Olimbitsa Thupi

❐ Galamukani!, 6/8/2005

Kodi Mumafunikadi Kuchita Zinthu Zolimbitsa Thupi?

Kodi Mumachita Mokwanira Zinthu Zolimbitsa Thupi?

Masewero a Yoga​—⁠Kodi Ndi Ongolimbitsa Thupi Chabe Kapena Pali Zinanso? Nsanja ya Olonda, 8/1/2002

Zakudya Zopatsa Thanzi

Kuthana ndi Vuto la Kunenepa Kwambiri Galamukani!, 10/2012

❐ Galamukani!, 6/2012

Kodi Zakudya Zanu N’zosamalidwa Bwino?

1. Muzisamala Pogula Zakudya

2. Muziyesetsa Kukhala Aukhondo

3. Muziphika Komanso Kusunga Chakudya Pamalo Abwino

4. Muzisamala Mukamadya Kulesitanti

Posachedwapa Aliyense Azidzadya Zakudya Zosamalidwa Bwino

Kodi Kusala Kudya Kumathandiza Munthu Kuyandikira kwa Mulungu? Nsanja ya Olonda, 4/1/2009

Kodi Pagona Vutoli Mpati, Nanga Kuipa Kwake N’kotani? Galamukani!, 3/8/2003

Chakudya Chopatsa Thanzi N’chosasowa Galamukani!, 5/8/2002

Kugona

❐ Galamukani!, 2/8/2004

Kodi Vuto la Kugona Tulo Tosakwanira Likukulirakulira?

Mmene Mungapezere Tulo Tokwanira

Kuzindikira Matenda Atulo Aakulu

❐ Galamukani!, 4/8/2003

Kodi Kugona N’kofunikadi Kapena Sikofunika Kwenikweni?

Zimene Mungachite Kuti Muzigona Bwino

Kodi Kuvutika Ndi Tulo kwa Achinyamata Ndi Nkhani Yodetsa Nkhaŵa? Galamukani!, 8/8/2002

Zimene Mungachite Mukamapanikizika Maganizo

Kumwetulira Ndi Mphatso Yofunika Kugawana Galamukani!, Na. 1 2017

Kodi Mungatani Ngati Mukuvutika Maganizo? Galamukani!, 5/2014

❐ Galamukani!, 6/2010

Kupanikizika N’koopsa Kwambiri

Kupanikizika Kumayambitsa Mavuto Aakulu

Zimene Tingachite Kuti Tisamapanikizike Kwambiri

Zimene Achinyamata Amadzifunsa: Kodi Ndingatani ndi Vuto la Kupanikizika Kusukulu? Galamukani!, 9/2008

❐ Galamukani!, 2/8/2005

Kusowa Mtendere Chifukwa cha Moyo Wopanikizika

Zimene Zimachititsa Moyo Kukhala Wopanikizika ndi Zotsatirapo Zake

Pali Zimene Mungachite Kuti Moyo Wanu Usakhale Wopanikizika

Mankhwala Omwe Angathandize Kuthetsa Nkhawa Nsanja ya Olonda, 12/15/2001

Thandizo Lachipatala

Zimene Owerenga Amafunsa: Kodi a Mboni za Yehova Amalandira Chithandizo Chachipatala? Nsanja ya Olonda, 2/1/2011

❐ Galamukani!, 6/8/2001

Thanzi Labwino kwa Onse​—Kodi Zingatheke?

Sayansi Yamakono ya Zamankhwala​—⁠Kodi Ingafike Pati?

Thanzi Labwino kwa Onse​—Lifika Posachedwapa!

Zimene Baibulo Limanena: Kusankha Chithandizo cha Mankhwala​—⁠Kodi N’kofunikira? Galamukani!, 1/8/2001

Kusamalira Thanzi M’njira Yogwirizana ndi Malemba

Yehova Adzakuthandizani Pamene Mukudwala Nsanja ya Olonda, 12/15/2015

Pitirizani Kuyandikira Yehova (Kamutu: Thanzi) Nsanja ya Olonda, 1/15/2013

Samalirani Thanzi Lanu M’njira Yogwirizana ndi Malemba Nsanja ya Olonda, 11/15/2008

Njira Zina Zochizira Matenda

Muziganiza Bwino Kwambiri (Kamutu: Nkhani Zokhudza Umoyo) Nsanja ya Olonda, 3/1/2006

Kodi Mankhwala Ochokera ku Zitsamba Angakuthandizeni? Galamukani!, 1/8/2004

Zimene Baibulo Limanena: Kodi Akristu Azichita Zogodomalitsa Maganizo? Galamukani!, 7/8/2003

❐ Galamukani!, 11/8/2000

Thanzi Labwino​—⁠Kodi Lingapezeke Mwanjira Zochiritsira Zatsopano?

Njira Zochiritsira Zosagwiritsidwa Ntchito Masiku Onse​—⁠Chifukwa Chomwe Anthu Ambiri Amazigwiritsira Ntchito

Kupenda Njira Zochiritsira Zosagwiritsidwa Ntchito Masiku Onse

Chosankha Chanu pa Chithandizo Chamankhwala

Matenda Ndiponso Mmene Thanzi la Munthu Lilili

Nkhanizi zikungofotokoza mfundo zosiyanasiyana zokhudza matenda osiyanasiyana ndipo cholinga chake sikupereka mankhwala kapena njira yochizira matenda. Munthu aliyense ayenera kuganiza mosamala asanapange chosankha pa nkhani ya thandizo lamankhwala, logwirizana ndi mfundo za m’Baibulo, limene akufuna kulandira.

Zambiri mwa nkhanizi ndi zochokera pa zimene anthu amene anakumana ndi vutolo ananena ndipo zingalimbikitse anthu ena amene akukumananso ndi vuto lomwelo.

Zimene Muyenera Kudziwa Zokhudza Matenda a Muubongo Galamukani!, 12/2014

Kodi Ndinalakwa Chiyani Kuti Ndidwale Chonchi? Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri, mutu 8

Zimene Mungachite Munthu Amene Mumakonda Akadwala Misala Galamukani!, 12/8/2004

Nkhondo Yakalekale Yofuna Kupeza Thanzi Labwino Galamukani!, 6/8/2004

Mafunso Ochokera kwa Owerenga: Munthu akamva mawu koma osaona amene akulankhula, kodi ndiye kuti sichinanso koma ziwanda n’zimene zikum’vutitsa? Nsanja ya Olonda, 5/1/2003

Ziphuphu Pathupi la Munthu

‘Kodi Chikuchitika N’chiyani M’thupi Mwangamu?’ Galamukani!, 7/8/2004

Edzi

❐ Galamukani!, 12/8/2004

Mankhwala a Edzi Akufunika Kwambiri!

Zinthu Zolimbikitsa Zimene Zachitika pa Ntchito Yolimbana ndi Edzi

Kodi Edzi Idzatha Liti?

❐ Galamukani!, 11/8/2002

“Sipanakhaleko Mliri Wosakaza Kwambiri Chonchi N’kale Lonse”

Edzi Yafala mu Africa

Ngati Mliri wa Edzi Udzagonjetsedwe, Kodi Ungadzagonjetsedwe Bwanji?

Ziwerengero Zochititsa Mantha za AIDS! Galamukani!, 3/8/2001

Amayi Odwala AIDS Akusowa Pogwira Galamukani!, 1/8/2000

Alubino

Vuto Lokhala Alubino Galamukani!, 7/2008

Matenda Obwera Chifukwa Chodana ndi Zinazake

Kodi Kudana ndi Kusagwirizana ndi Zakudya kwa Thupi N’kosiyana Bwanji? Galamukani!, Na. 3 2016

N’chifukwa Chiyani Anthu Ambiri Amadwala Chimfine Chimene Chimabwera Akakhala Pafupi ndi Mungu? Galamukani!, 6/8/2004

Matenda Otchedwa Alzheimer

“Mwina Nyimbo Ndi Imene Ingathandize” Galamukani!, 9/2010

Matenda Opha Ziwalo Otchedwa Amyotrophic Lateral Sclerosis (ALS)

Matendawa amatchedwanso matenda a Lou Gehrig

Mabanja Amene Zinthu Zikuwayendera Bwino​—Chigawo Chachiwiri (Kamutu: Ngati Wina M’banja Mwanu Akudwala Matenda Aakulu) Galamukani!, 10/2009

Chikhulupiriro Chandithandiza Kupirira Matenda Oopsa Galamukani!, 1/2006

Matenda a Kuda Nkhawa

Kodi Mungatani Kuti Muthandize Odwala Matenda Oda Nkhawa? Galamukani!, 3/2012

❐ Galamukani!, 9/8/2001

Pamene Mwakumana ndi Zoopsa

Kodi Vuto Lokhala Wamantha Mukamakumbukira Zoopsa Ndi Lotani Kwenikweni?

Vuto la Mantha Lidzatha!

Nyamakazi

❐ Galamukani!, 12/8/2001

Nyamakazi Ndi Matenda Opundula Anthu

Kuwadziwa bwino Matenda a Nyamakazi

Odwala Nyamakazi Asataye Mtima

Matenda Otchedwa Asperger

Kulimbana ndi Matenda a Asperger Galamukani!, 9/2008

Khungu

Amachita Zinthu Bwinobwino Ngakhale Kuti Ndi Osaona Galamukani!, 11/2015

Baibulo Limasintha Anthu: Panopa Ndimaona Kuti Ndingathe Kuthandiza Ena Nsanja ya Olonda, 10/1/2015

“Ngati Kingsley Akukwanitsa, Kuli Bwanji Ine?” Nsanja ya Olonda, 6/15/2015

Muzithandiza Anthu Osaona Kudziwa za Yehova Utumiki wa Ufumu, 5/2015

Ndimakonda Nyimbo, Moyo, ndi Baibulo Galamukani!, 8/2007

Kodi Muli ndi Vuto Losiyanitsa Mitundu? Galamukani!, 7/2007

Ndinalandira ‘Zokhumba Mtima Wanga’ Nsanja ya Olonda, 11/1/2005

Maso Anga Anatseguka Ngakhale Kuti Ndinali Wakhungu! Nsanja ya Olonda, 5/1/2004

Matenda Otchedwa Body Dysmorphic Disorder (BDD)

❐ Galamukani!, 1/8/2005

Kuipa Kofunitsitsa Kukhala Wokongola

Kukongola Kofunika Kwambiri

Nkhawa Imene Munthu Ali Nayo pa Maonekedwe Ake Ikasanduka Matenda Galamukani!, 8/8/2004

Matenda Amene Anayamba ndi Makoswe (The Black Death)

Mliri wa Matenda a Makoswe​—Unakantha Ulaya M’Nyengo Zapakati Galamukani!, 2/8/2000

Kupanikizika ndi Ntchito

Kodi Mungatani Ngati Mukupanikizika Chifukwa cha Ntchito? Galamukani!, 9/2014

Khansa

Zimene Mungachite Ngati Mwapezeka ndi Khansa ya M’mawere Galamukani!, 8/2011

Zimene Makolo Angachite Ngati Mwana Wawo Ali ndi Khansa Galamukani!, 5/2011

❐ Galamukani!, 6/8/2005

Maganizo a Anthu Asintha pa Nkhani ya Khungu Ayamba Kufuna Khungu Loderako Osati Loyera

Tetezani Khungu Lanu

Kupirira ndi Khansa Yapakhungu

Matenda a Muubongo Olumalitsa Ziwalo (Cerebral Palsy)

Jairo Amagwiritsa Ntchito Maso Ake Kutumikira Mulungu Nsanja ya Olonda, 3/1/2015

Loida Ayamba Kulankhula Galamukani!, 5/8/2000

Matenda Ofanana ndi Kaodzera (Chagas’ Disease)

Matenda Ofalitsidwa ndi Tizilombo Akuvutitsa Kwambiri Galamukani!, 6/8/2003

Ntchofu

Ngati Mwana Wanu Wakhanda Sasiya Kulira Galamukani!, 5/8/2004

Matenda Otchedwa Cystic Fibrosis

Chikhulupiriro Chake Chimalimbikitsa Ena Nsanja ya Olonda, 7/1/2006

Kukhala Wogontha

Onani mutu wakuti Maphunziro ndi Chinenero ➤ Chinenero Chamanja

Matenda a Chingwangwa

Matenda a Chingwangwa Avuta Kwambiri Galamukani!, 11/2011

Matenda a Maganizo ndi Kuvutika Maganizo

N’chifukwa Chiyani Achinyamata Ambiri Akudwala Matenda Ovutika Maganizo? Galamukani!, Na. 1 2017

Zimene Muyenera Kudziwa Zokhudza Matenda a Muubongo Galamukani!, 12/2014

Zimene Baibulo Limanena: Kuvutika Maganizo Galamukani!, 10/2013

Yandikirani Mulungu: Nkhani Yolimbikitsa kwa Anthu Osweka Mtima Nsanja ya Olonda, 6/1/2011

❐ Galamukani!, 7/2009 Kodi Matenda Ovutika Maganizo Ndi Otani?

Kodi Mungathetse Bwanji Matenda Ovutika Maganizo?

“Mulungu wa Chitonthozo Chonse” Amathandiza

Musaope Yehova Ali Nanu Nsanja ya Olonda, 5/1/2006

❐ Galamukani!, 1/8/2004

Anthu Osautsika Maganizo

Kukhala ndi Matenda a Maganizo

Nkhani Yabwino kwa Odwala Matendawa

Mmene Ena Angathandizire

❐ Galamukani!, 9/8/2001

Msinkhu Umene Uli Patsoka Lalikulu

Kudziwa Zizindikiro Zake

Kudziwa Zoyambitsa Zake

Mmene Mungathandizire

“Simudziwa Chimene Chidzagwa Mawa” Nsanja ya Olonda, 12/1/2000

Matenda a Shuga

Zimene Mungachite Kuti Mupewe Matenda a Shuga Galamukani!, 9/2014

❐ Galamukani!, 5/8/2003

Matenda a Shuga “Amapha Mosadziwika”

Vuto la Chithandizo Chake

Mmene Baibulo Lingathandizire Odwala Matendawa

Kulumala

Ndilibe Manja Koma Ndinatha Kulandira Choonadi cha M’Baibulo Nsanja ya Olonda (Yogawira), Na. 6 2016

Chinsinsi cha Banja Losangalala: Zimene Mungachite Ngati Mkazi Kapena Mwamuna Wanu Ali ndi Matenda Aakulu Nsanja ya Olonda, 11/1/2009

Kuthandiza Ana Amene Ali ndi Vuto Lophunzira Galamukani!, 1/2009

Kulera Ana Omwe Amafunika Kuwasamalira Mwapadera Galamukani!, 4/2006

Kukaona Malo Opangira Ziwalo Galamukani!, 2/2006

Kulumala N’kosiyanasiyana Nsanja ya Olonda, 5/1/2002

Matenda a Kuzerezeka

Kulera Ana Obadwa ndi Matenda Ozerezeka Galamukani!, 6/2011

Mavuto Amene Takumana Nawo Atithandiza Kudalira Yehova Nsanja ya Olonda, 4/15/2010

Matenda Akukhala Wamfupi Kwambiri

Matupi Aang’ono, Mitima Yabwino Nsanja ya Olonda, 2/15/2000

Matenda a Kuvutika Kudya

Kodi Ndingatani Ngati Sindikusangalala ndi Mmene Ndikuonekera? (Kamutu: Chenjerani ndi Vuto Lodana ndi Chakudya) Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri, mutu 7

Zimene Achinyamata Amadzifunsa: Kodi Ndili Ndi Matenda Ovutika Kudya? Galamukani!, 10/2006

Kufuna Kuoneka Bwino Kuli M’poipira Pake Galamukani!, 9/8/2003

Matenda Akugwa

Zimene Muyenera Kudziwa Ponena za Matenda a Khunyu Galamukani!, 10/2013

Ndinafunitsitsa Kukwanitsa Cholinga Changa Galamukani!, 7/8/2005

Matenda Okomoka

Bwanji Ndimakomokakomoka? Galamukani!, 4/2007

Kutentha Thupi

Mwana Wanu Akatentha Thupi Galamukani!, 12/8/2003

Kusagwirizana ndi Chakudya

Kodi Kudana ndi Kusagwirizana ndi Zakudya kwa Thupi N’kosiyana Bwanji? Galamukani!, Na. 3 2016

Nyamakazi ya M’mafupa

Kodi Nyamakazi ya M’mafupa Imayamba Bwanji? Galamukani!, 8/2012

Chiseyeye

Zimene Mungachite Kuti Mupewe Chiseyeye Galamukani!, 6/2014

Mutu

Kodi Mungatani Ngati Mumadwala Mutu Waching’alang’ala? Galamukani!, 1/2011

Matenda Otupa Chiwindi

Matenda Otupa Chiwindi Amapha Mwakabisira Galamukani!, 8/2010

Matenda a Kuthamanga kwa Magazi

Kuteteza Ndiponso Kuletsa Matenda a Kuthamanga kwa Magazi Galamukani!, 5/8/2002

Matenda Otchedwa Huntington (HD)

Nthenda Yotchedwa Huntington​—Tidziwe Bwino Tsoka Lachibadwa Limeneli Galamukani!, 4/8/2000

Chimfine

Tetezani Banja Lanu ku Matenda a Chimfine Galamukani!, 6/2010

Matenda Ofalitsidwa ndi Tizilombo

❐ Galamukani!, 6/8/2003

Matenda Ofalitsidwa ndi Tizilombo Akuvutitsa Kwambiri

N’chifukwa Chiyani Ayambiranso?

Kodi Zinthu Zidzasintha?

Matenda a Kusowa Tulo

Onani Thanzi ➤ Kukhala ndi Thanzi Labwino ➤ Kugona

Matenda a M’chikodzodzo

❐ Galamukani!, 3/8/2001

Kulimbana ndi Matenda Ofoola Thupi

Poizoni

Samalani ndi Poizoni Galamukani!, 12/2009

Vuto Lophunzira

Kuthandiza Ana Amene Ali ndi Vuto Lophunzira Galamukani!, 1/2009

Khate

Kodi Mukudziwa? (Kamutu: Kodi Yesu ankasiyana bwanji ndi Arabi pochita zinthu ndi anthu akhate?) Nsanja ya Olonda (Yogawira), Na. 4 2016

Kodi Mukudziwa? (Kamutu: Kodi matenda a khate omwe amafotokozedwa m’Baibulo ndi ofanana ndi khate la masiku ano?) Nsanja ya Olonda, 2/1/2009

Matenda Ofalitsidwa ndi Nthata Omwenso Amayambitsa Nyamakazi (Lyme Disease)

N’chifukwa Chiyani Ayambiranso? Galamukani!, 6/8/2003

Malungo

Kodi Mukudziwa Zotani pa Nkhani ya Malungo? Galamukani!, 7/2015

Matenda a Kusowa Zakudya M’thupi

❐ Galamukani!, 3/8/2003

Mliri Woopsa Kwambiri

Kodi Pagona Vutoli Mpati, Nanga Kuipa Kwake N’kotani?

“Mliri Wobisikawu” Utha Posachedwa!

Matenda Osiya Kusamba

Kupirira Mavuto Amene Azimayi Amakumana Nawo Akamasiya Kusamba Galamukani!, 11/2013

Matenda Oti Thupi Siligwirizana ndi Kuphatikiza Mankhwala Osiyanasiyana (MCS)

Mafunso Ochokera kwa Owerenga: Kodi tingathandize bwanji abale ndi alongo amene amavutika akamva fungo la perefyumu? Nsanja ya Olonda, 2/15/2015

❐ Galamukani!, 8/8/2000

Mukadwala Chifukwa cha Mankhwala

Kuthandiza Anthu Odwala MCS

Kunenepa Kwambiri

Kodi Mungatani Kuti Mwana Wanu Asanenepe Kwambiri? Galamukani!, 3/2009

❐ Galamukani!, 11/8/2004

Kodi Kunenepa Kwambiri Ndi Vutodi?

Kodi N’chiyani Chimachititsa Anthu Kunenepa Kwambiri?

Kodi Kunenepa Kwambiri Mungakuthetse Bwanji?

Kodi Kuchita Khama Kuti Muchepetse Kunenepa N’kwaphindudi?

Matenda Omwe Amachititsa Kuti Mafupa Akhale Ofewa Kwambiri (Osteogenesis Imperfecta)

Matendawa amatchedwanso, brittle bone

Kutumikira Mulungu Kuli Ngati Mankhwala Ake Nsanja ya Olonda, 11/15/2013

Ndikusangalala Ngakhale Kuti Ndine Wolumala Nsanja ya Olonda, 5/1/2009

Matenda Ofooketsa Mafupa (Osteoporosis)

Matenda Ofooketsa Mafupa Amayamba Mosaonekera Galamukani!, 6/2010

Kufa Ziwalo

Yehova Wandichitira Zazikulu Nsanja ya Olonda, 8/1/2015

Poliyo

Kusangalala Nawo “Moyo Uno” Nsanja ya Olonda, 6/1/2005

Vuto la Kusokonezeka Maganizo Pambuyo Pobereka

Ndinagonjetsa Vuto Langa Losokonezeka Maganizo Nditabereka Galamukani!, 8/8/2002

Matenda a Pulositeti

Zimene Mungachite Ngati Muli ndi Matenda a Pulositeti Galamukani!, 2/2011

Matenda Otchedwa Rett

Salankhula Koma Timamvana Galamukani!, 10/2008

Matenda a Scleroderma

“Ndimayesetsa Kuti Ndisamangoganizira za Matenda Anga” Galamukani!, 1/2015

Matenda Opindika Msana

Sanasiye Kutsatira Zimene Amakhulupirira Galamukani!, 8/2015

Vuto la Kudwala Chifukwa cha Kusintha kwa Nyengo (SAD)

Nyengo Imene Dzuwa Silituluka Galamukani!, 12/2008

Kudzivulaza

Kodi Achinyamata Amakumana ndi Mavuto Otani? (Bokosi: Achinyamata Akudzipweteka) Galamukani!, 9/2009

Zimene Achinyamata Amadzifunsa: Kodi Ndingatani Kuti Ndisiye Kudzivulaza? Galamukani!, 2/2006

Zimene Achinyamata Amadzifunsa: N’chifukwa Chiyani Ndimadzivulaza? Galamukani!, 1/2006

Matenda Olumala Msana

Yehova ‘Amanyamula Katundu Wanga Tsiku ndi Tsiku’ Nsanja ya Olonda, 8/15/2013

Kuvulala Msana

Yehova Anandithandiza pa Nthawi Yomwe Ndinkafunikiradi Kuthandizidwa Galamukani!, 11/2014

Zilonda za M’mimba

Banja Liyesedwa Chikhulupiriro Galamukani!, 5/8/2004

Matenda a Vitiligo

Matenda Osintha Mtundu wa Khungu Galamukani!, 10/8/2004

Kukhala Woyembekezera, Kubereka ndi Kusamalira Mwana

Abale a m’Komiti Yolankhulana ndi Achipatala angapereke kwa madokotala kabuku kokhala ndi njira zosiyanasiyana zochizira odwala popanda kuwaika magazi. Funsani akulu a mumpingo mwanu kuti mudziwe zambiri.

Mafunso Ochokera kwa Owerenga: Kodi Akhristu angagwiritse ntchito lupu (IUD) ngati njira ya kulera? Nsanja ya Olonda (Yophunzira), 12/2017

Zithunzi Zakale: Ignaz Semmelweis Galamukani!, Na. 3 2016

Zimene Mungachite Mwana Akabadwa Banja Losangalala, chigawo 6

Mwana Akamabadwa Pamachitika Zodabwitsa Galamukani!, 1/2011

Mayi Wathanzi Amaberekanso Mwana Wathanzi Galamukani!, 11/2009

Mmene Kumwa Mowa Mopitirira Muyeso Kumakhudzira Thanzi la Munthu Galamukani!, 10/8/2005

❐ Galamukani!, 10/8/2004

Ana Ambiri Akubadwa Kudzera M’njira Zothandizira Anthu Osabereka Kuti Abereke

Njira Zatsopanozi Zabweretsanso Mavuto Atsopano

Mmene Mungatetezere Pathupi Panu Galamukani!, 1/8/2003

Ukalamba

Onaninso mutu wakuti Moyo Wachikhristu ➤ Kuthandiza Abale Athu ➤ Okalamba

Mungatani Kuti Muzisangalalabe Ngakhale Mutakalamba? Nsanja ya Olonda, 6/1/2015

❐ Nsanja ya Olonda, 6/1/2006

N’ngokalamba Koma Amanyalanyazidwa ndi Kuzunzidwa

Mulungu Amasamalira Okalamba

N’chifukwa Chiyani Timakalamba? Galamukani!, 5/2006

❐ Galamukani!, 2/2006

Kodi Ukalamba Ungakhaledi Wosangalatsa?

Kupirira Mavuto a Ukalamba

Kukhala ndi Mphamvu Ngati Wachinyamata Mpaka Muyaya

Anthu Akuona Ukalamba Mosiyana ndi Kale Galamukani!, 9/8/2001

Kukalambirana Chinsinsi cha Banja, mutu 14

Kusamalira Odwala

Mungatani Ngati Munthu Amene Mumamukonda Akudwala Matenda Oti Sachira? Nsanja ya Olonda (Yogawira), Na. 4 2017

Kodi Mungathandize Bwanji Mnzanu Kapena Wachibale Akadwala? Galamukani!, 10/2015

Khalanibe Olimba Mwauzimu Mukamasamalira Wachibale Amene Akudwala Nsanja ya Olonda, 5/15/2010

Chinsinsi cha Banja Losangalala: Zimene Mungachite Ngati Mkazi Kapena Mwamuna Wanu Ali ndi Matenda Aakulu Nsanja ya Olonda, 11/1/2009

Madokotala Amakumana N’zambiri Galamukani!, 2/8/2005

❐ Galamukani!, 6/8/2000

Pamene Nthenda Yaikulu Yagwira Banja

Matenda Aakulu Ndi Nkhani ya Banja Lonse

Mmene Mabanja Amapiririra Matenda Aakulu

Nthenda Yotchedwa Huntington​—Tidziwe Bwino Tsoka Lachibadwa Limeneli (Kamutu: Kuthandiza Osamala Odwala) Galamukani!, 4/8/2000

Pamene Wina M’banja Wadwala Chinsinsi cha Banja, mutu 10

Zizolowezi Zoipa

Onani mutu wakuti Dziko la Satana ➤ Zizolowezi Zoipa

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena