Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w15 6/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 6/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

June 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

JULY 27, 2015–AUGUST 2, 2015

Khristu Ndiye Mphamvu ya Mulungu

TSAMBA 3 • NYIMBO: 14, 109

AUGUST 3-9, 2015

Yesu Amakonda Anthu

TSAMBA 8 • NYIMBO: 84, 99

AUGUST 10-16, 2015

N’zotheka Kukhalabe Oyera

TSAMBA 13 • NYIMBO: 83, 57

AUGUST 17-23, 2015

Tizichita Zinthu Mogwirizana ndi Pemphero la Ambuye—Gawo I

TSAMBA 20 • NYIMBO: 138 (nyimbo yatsopano yakuti Inu Ndinu Yehova), 89

AUGUST 24-30, 2015

Tizichita Zinthu Mogwirizana ndi Pemphero la Ambuye—Gawo 2

TSAMBA 25 • NYIMBO: 22, 68

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Khristu Ndiye Mphamvu ya Mulungu

▪ Yesu Amakonda Anthu

Nkhanizi zikufotokoza zozizwitsa za Yesu ndipo zikusonyeza zimene tingachite potsanzira mtima wake wopatsa komanso wachifundo. Zikufotokozanso makhalidwe ena abwino a Yesu. Nkhanizi zitithandizanso kudziwa kuti posachedwapa tidzaona zozizwitsa zikuchitika padziko lonse.

▪ N’zotheka Kukhalabe Oyera

M’dzikoli, kukhala oyera si chinthu chapafupi. Nkhaniyi ikufotokoza zinthu zimene zingatithandize kupewa maganizo oipa n’kumatsatira mfundo zapamwamba za Yehova. Zinthu zake ndi kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova, kutsatira malangizo a m’Baibulo ndiponso kulola kuti Akhristu anzathu atithandize.

▪ Tizichita Zinthu Mogwirizana ndi Pemphero la Ambuye—Gawo I

▪ Tizichita Zinthu Mogwirizana ndi Pemphero la Ambuye—Gawo 2

Akhristu saloweza pemphero la Ambuye kuti azilinena mobwerezabwereza. Koma tikhoza kuphunzira zambiri pa mfundo za m’pempheroli. Nkhanizi zitithandiza kuti tizichita zinthu mogwirizana ndi pemphero limeneli.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

18 “Ngati Kingsley Akukwanitsa, Kuli Bwanji Ine?”

30 “Mukufunika Kupirira”

32 Kodi Mukukumbukira?

PATSAMBA LOYAMBA: A Mboni akwera maboti kuti akalalikire pazilumba za kumpoto chakumadzulo kwa Panama. Ayenera kulalikira anthu ena m’chilankhulo cha Chinobele

PANAMA

KULI ANTHU

3,931,000

KULI OFALITSA

16,217

KULI APAINIYA OKHAZIKIKA

2,534

Ku Panama kuli mipingo 309 ndiponso apainiya apadera oposa 180. Kuli ofalitsa pafupifupi 1,100 m’mipingo 35 yachinobele ndiponso timagulu 15. Kulinso ofalitsa pafupifupi 600 m’mipingo 16 yachinenero chamanja cha ku Panama ndiponso timagulu 6

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena