Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/97 tsamba 7
  • “Ndani Adzatimukira Ife?”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ndani Adzatimukira Ife?”
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—1997
  • Nkhani Yofanana
  • Madalitso a Utumiki Waupainiya
    Nsanja ya Olonda—1997
  • Kodi Mungawonjezere Zimene Mumachita mu Utumiki?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Mtima Wodzipereka Umabweretsa Madalitso
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2007
  • Utumiki Waupainiya—Kodi Ngoyenera Inu?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1998
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—1997
km 7/97 tsamba 7

“Ndani Adzatimukira Ife?”

Yehova atafunsa funso limeneli, Yesaya anayankha mwamsanga kuti: “Ndine pano; munditumize ine.” (Yes. 6:8) Popeza pali zambiri zofuna kututa lerolino, chiitanocho chikuperekedwa tsopano. Antchito a nthaŵi zonse owonjezereka—apainiya okhazikika—akufunika mwamsanga! (Mat. 9:37) Kodi mukufuna kudzipereka? Ngati zili choncho, September 1, kuyamba kwa chaka chautumiki cha 1998, idzakhala nthaŵi yabwino yoloŵera upainiya. Bwanji osapempha fomu yofunsirapo kwa akulu?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena