Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/10 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 8

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 8
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 8
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 3/10 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa March 8

MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 8

Nyimbo Na. 20

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 4 ndime 12-21 ndi bokosi la patsamba 42a

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Samueli 1-4

Na. 1: 1 Samueli 2:​18-29

Na. 2: Kodi Yesu Anaphunzitsa Kuti Oipa Amazunzidwa Akamwalira? (rs tsa.149 ndime 6)

Na. 3: Malemba Amasonyeza Kuti Yehova Amakonda Ana

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 5

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kodi Mukamalalikira Uthenga wa m’Baibulo Mumalankhula Momveka? Nkhani yochokera mu buku la Sukulu ya Utumiki, kuyambira patsamba 109, ndime 2 mpaka kumapeto kwa mutuwo.

Mph. 20: “Zimene Tingachite Poyamikira Mphatso Yaikulu Kwambiri Imene Mulungu Anatipatsa.” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho. Mukatha kukambirana ndime 3, fotokozaninso zimene mpingowo wakonza pantchito yapadera yogawira timapepala toitanira anthu ku Chikumbutso. Pemphani mpainiya wothandiza kuti achite chitsanzo cha mmene angagawirire kapepala koitanira anthu ku Chikumbutso. Akatha, m’funseni kuti anene zimene anachita kuti apeze nthawi yochita upainiya wothandiza komanso anene mmene wapindulira.

Nyimbo Na. 8

[Mawu a M’munsi]

a Mungasankhe kukambirana bokosi kapena ayi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena